TN Stars, Savenda Chitipa United relieved - The Times Group Malawi Football Association of Malawi (Fam) First Instance Body (FIB) has finally granted licences to TN Stars and Savenda Chitipa... times.mw
Blue Eagles says it's disappointed on last minute postponement of TNM Super League by the Super League of Malawi (Sulom) considering of resources spent on their trip to Blantyre.
Mwini wake wa Ntopwa, Isaac Jomo Osman, wapereka ndalama ya chikole ku FAM yokwana 1 million Kwacha.
Osman wachita izi potsatira mfundo za Club Licensing kuti alandire chiphaso cha ndondomeko-yi.
Matimu omwe amasewera mu ligi ya TNM m'masewero a koyenda aononga ndalama pomwe tsiku loyamba masewero mu ligi-yi silikudziwika kutsatira kusinthidwa kwa masiku.
Football Association of Malawi and Super League of Malawi have with immediate effect suspended football matches in Malawi following the ban of more than 100 people gathering by President Mutharika.
Fischer Kondowe ati wachita kupangilidwa chiganizo kuti asiye kusewelera ku Bullets pomwe timuyi inalibe chidwi choonjezera kontrakiti yake.
BE FORWARD Wanderers have signed Juma Yatina and Wisdom Mpinganjira.
Yatina has signed a 3 year contract while Mpinganjira has seal a 3 year deal with the Nomads.
Five BE FORWARD Wanderers players have extended their stay at the club.
The five are; Alfred Manyozo, Lucky Malata, Stanley Sanudi, Isaac Kaliati and Richard Chipuwa.
MAFCO have arrived in Karonga ahead of their two away TNM Super League games this weekend.
Head Coach for the team, Stereo Gondwe, has confirmed the development to Owinna.
Patsogolo potsegulira mpikisano wa TNM Super League, aphunzitsi a matimu mu ligi-yi ati akonzeka kuchita bwino chaka chino.
Aphunzitsi a matimu a MAFCO, Bullets komanso Wanderers ndiwo anena izi.