Bungwe la FAM latsimikiza kuti silionjezera mgwirizano wake ndi mphunzitsi wa timu ya Flames Mario Marinica ukatha pa 30 April.
Kalata yomwe mlembi wa FAM Alfred Gunda walemba yatsindika za chikonzerochi
FAM yati izamukumbukira Marinica popanga mbiri komanso kubweletsa chimwemwe pamene Malawi inafika koyamba mu Round of 16 ku AFCON imene inaseweledwa ku Cameroon chaka chatha.
Login with Facebook to post predictions, updates & live scores