Malawi President, Peter Mutharika, who once played as centre half has pledged to buy new buses for Nyasa Big Bullets and BE FORWARD Wanderers.
The construction of Nyasa Big Bullets and BE FORWARD Wanderers stadiums will be completed in the next 78 weeks.
Minister of Sports, Francis Phiso, has confirmed the development.
Mlembi wa masapota wa timu ya BE FORWARD Wanderers, Samuel Mponda, wachenjeza anthu kuti asawatchingire pamene ali ndi lingaliro lopempha thandizo la ndalama kwa mtsogoleri wa dziko lino.
Aliyense owina pa masewero omwe amachititsa a Premier Bet ati kuyambira tsopano akuyenera kumalipira msonkho ku boma.
President Peter Mutharika will today launch the commencement of construction of Nyasa Big Bullets and BE FORWARD Wanderers stadiums in Blantyre.
Local football teams will be allowed to buy a duty free 26 seater bus outside the country once every five years.
Northern Region Youth Football Committee (NRYFC) has advised all district youth committees and club's to not resume football until a communication is made from Football Association of Malawi (FAM).
Mphunzitsi wa timu ya Karonga United, Dan Dzikambani, wapempha bungwe la FAM kufulumizitsa ndondomeko yoti masewero a mpira ayambe mdziko muno.
Bungwe la FAM alipempha kuti like ndondomeko zoonetsetsa kuti masewero a mpira asamakhudzidwe ndi nyengo ya mvula pomwe tsopano sizoni iziyamba mu August.
Football Association of Malawi (FAM) will next week finalise giving out the Covid-19 relief package to all stakeholders.