Login with Facebook to post predictions, updates & live scores
Nyasa big
Mamelodi fire
I love you noma
Football Association of Malawi (FAM) has appointed Flames Assistant coach and Under 20 Head Coach Patrick Mabedi as Flames Caretaker coach until September 2023.
Mighty Mukuru Wanderers yesterday evening entered into a one-year agreement with Smile Life Insurance Company.
The deal that will see the company, sponsoring man of the match award for the club in every League and Cup games played to the tune of K150,000.
First player to receive the K150,00 from Smile Life Insurance Company Man of the Match award was Christopher Kumwembe.
Kumwembe was named man of the match during a league opener against Civo Service United at the Kamuzu stadium over the weekend.
Bungwe loyendetsa masewero a mpira wa miyendo mdziko muno la Football Association of Malawi (FAM) likuyembekezeka kulemba ntchito mphunzitsi ongogwirizira wa timu ya Malawi kumathero a sabata lino.
Izi ndi malingana ndizomwe yalemba nyuzipepa ya Times lero.
FAM inalengeza kuti sionjezera mgwirizano wake ndi mphunzitsi wa ku Romania, Mario Marian Marinica yemwe mgwirizano wake ukutha kumathero kwa mwezi uno.
FAM ikuyembekezereka kukasankhanso anthu ena mu komiti yoona za kagwiridwe ntchito ka mphunzitsi kapena kuti Sub-technical committee omwe akalowe mmalo mwa Tiya Somba Banda ndi Sugzo Ngwira.
A Tiya Somba Banda anagonja pa masankho a Bungwe la Super League of Malawi, Sulom ndi Fleetwood Haiya.
Sugzo Ngwira wagonja pa masankho a National Women's Football Association pamaso pa Adelaide Migogo.
Ernesto, sapota wa Manoma, wawina K10,000πΈ atalosera molondolaπ― magemu 5 pa owinna.comβ½π
Loserani magemu ambiri pa Owinna.com kuti nanunso mukhale ndi mwayi wowina ndalamazi.
Tatumiza. Congrats π
Ndathokoza ndalandila k10,000 yanga zikomo.
Nyelele mbambande
Thank you Davie
The Super League of Malawi has confirmed that FCB Nyasa Big Bullets match against MAFCO, which was originally scheduled for Saturday 22 April will be played on Sunday 23 April.
The Premier League have released a 40-player shortlist for the Team of the Season.
Kampani ya Castel kuyambira chaka chino ibweletsa chikho chatsopano chomwe chizitchedwa Castel Challenge Cup.
Matimu oposa 2000 ndi omwe atamakanganilane chikhochi kuchokera ku district mpaka national level. Ndalama zokwana 1 billion ndi zomwe zingagwilisidwe ntchito kwa zaka zitatu,MK320 million pachaka.
Katswiri wa chikhochi azilandira ndalama zokwana MK50 million.