TP MAZEMBE YANYAMUKA BWAKU MALAWI
Timu yaku Democratic Republic of Congo, ya TP Mazembe, yanyamuka kwawo kulowera mu dziko la mkaka ndi uchi, la Malawi patsogolo pa masewero awo ndi timu ya FCB Nyasa Big Bullets mu CAF Champions league pa bwalo la Bingu.
Timuyi yalengeza za ulendowu pa tsamba lawo la Facebook ndipo akuyembekezeka kufika mdziko muno maola akudzawa pomwe masewero aliko lamulungu likudzali.
#Tawonga2023
Login with Facebook to post predictions, updates & live scores