NTHALA ALI KU SOUTH AFRICA
Mphunzitsi wamagoloboyi kutimu ya Mighty Mukuru Wanderers, Simplex Nthala, ali mdziko la South Africa komwe akukaonjezera nzeru za maphunziro ku bungwe la COSAFA.
Nthala anapita mdzikoli sabata yatha ndipo akachitabe maphunzirowa pamodzi ndi anthu ena ammaiko akummwera kwa Africa.
Login with Facebook to post predictions, updates & live scores