DE JONGH WACHOKA KU SILVER
Mphunzitsi wa Silver Strikers, Peter De Jongh, wasiya ntchito yake kutimuyi pomwe akufuna akaone zina ku matimu ena.
Malingana ndi malipoti, mphunzitsiyu wauza akuluakulu atimuyi kuti athetse mgwirizano wawo kamba koti sali wokondwanso kukhala kutimuyi.
Uyu ndi mzungu wachiwiri kutsanzika kutimu kwake pomwe mphunzitsi wakale wa Mighty Mukuru Wanderers, Mark Harrison anatsanzika mwezi watha.
Login with Facebook to post predictions, updates & live scores