Goloboyi wakale wa timu ya dziko lino ya Flames, Boniface Maganga wamwalira.
A Maganga atisiya lero pa chipatala cha Queen Elizabeth mu mzinda wa Blantyre komwe amalandira thandizo la chipatala.
Maganga anali goloboyi wa Flames kuyambira chaka 1969 ndipo anali m'modzi mwa akatswiri omwe anathandiza Malawi kutenga chikho cha East and Central Africa Senior Challenge Cup mu 1978 ndi 1979.
To obituarise such an incredibly talented goalkeeper as a "goal boy" smacks of complete lack of respect to him and his family including all of us who watched him represent the country with excellence
#Boniface Maganga was one of the best and smartest goalkeepers in Malawi. Growing up in that era Maganga was a famous figure at Lubani Road. Every aspiring young goalkeepers wanted to be a "Boniface"
Login with Facebook to post predictions, updates & live scores