OYIMBIRA AKU MALAWI AOMBA M'GOLO
Bungwe la Confederation of African Football latulutsa ndandanda wa oyimbira omwe atumikire mmasewero akumpikisano wa African Cup of Nations womwe uyambe chaka cha mawa.
Mayinawa ndi makumi asanu ndi mmodzi mphambu zisanu ndi zitatu (68) ochokera mmayiko angapo komatu palibepo oyimbira angakhale mmodzi yemwe wasankhidwa kuchokera ku Malawi.
Izi zikudza pomwe tsopano pakutha zaka tsopano oyimbira amdziko lino asakutengedwa ku mipikisano ikuluilkulu pomwenso matimu ochuluka akumadandaula ndi kayimbilidwe ka oyimbirawa mmalawi.
Login with Facebook to post predictions, updates & live scores