BANGWE YATENGA MKANDAWIRE
Timu ya Bangwe All Stars yalengeza kuti yatenga mphunzitsi wakale watimu ya Scorchers, Abel Mkandawire, kuti aphunzitse timuyi kwa miyezi isanu ndi umodzi ikudzayi.
Timuyi yalengeza za nkhaniyi lero pomwe yati Joseph Kamwendo ndi yemwe akhale wachiwiri kwa mphunzitsiyu.
Bangwe ili pa nambala 12 mu ligi ya TNM pomwe ili ndi mapointsi okwana 18 pa masewero 17 omwe yasewera.
Ayitha koma ndawa coach anampeza afam e ay sakuyenela utelo akhoza umutenga
Login with Facebook to post predictions, updates & live scores