NAM ILI NDI MKUMANO WAUKULU
Bungwe loyendetsa mpira wa manja mdziko muno, la Netball Association of Malawi (NAM) lalengeza kuti mkumano wawo wawukulu wapachaka uliko lowerukali ku nyumba ya Civo ku Lilongwe kuyambira mmawa.
Bungwe lati mwazina, likasankha wachiwiri kwa mtsogoleri wa bungweli pomwe a Chimwemwe Bakali anatula pansi udindo wawo chaka Chatha.
Iwo akaunikiranso mmene ndalama zayendera mu chaka cha 2022 mpaka 2023 komanso kusankha anthu ofufuza mmene ziziyendera mu ntchito za bungweli.
Login with Facebook to post predictions, updates & live scores