Login with Facebook to post predictions, updates & live scores
Wosewera wotchinga pagolo wa Nyasa Big Bullets, Richard Chimbamba wayamikila ubale wabwino womwe ulipo pakati pa iye ndi timuyi kuyambira kumabwana komanso m'phunzitsi wa timuyi.
Chimbamba walankhula izi pamene Bullets yawonjezera gwilizana wake ndi iye kwazaka zina ziwiri.
Iye wati izi zimpatsa mangolomera atsopano ndipo watsimikiza kuti apitiliza kudzipeleka potumikila timu yake.
Powonjezera apa, Chimbamba wachenjeza onsewera anzake omwe akubwera kumene kutimuyi kuti ayenera kukhala amwambo kaamba kakuti izi ndizomwe zimathandizila kukhalitsa pa malo monga momwe zakhalira kwa iye ndi Bullets.
Peter Banda, Chiukepo Msowoya, Luke Chima and Richard Chimbamba have been included in Nyasa Big Bullets final squad travelling to the northern region.
Players contesting the player of the month award for August: 1. Deus Nkutu - Moyale Barracks 2. John Soko - Blue Eagles 3. Richard Chimbamba - Ntopwa 4. Willie Sayenda - Mighty Tigers.