Login with Facebook to post predictions, updates & live scores
Yamikani Chester set to light up Las Vegas - The Times Group Malawi Malawi national football team attacker Yamikani Chester has said he is motivated to deliver for his United States League (USL)... times.mw
Manchester-city
FAM BOSS NYAMILANDU PLAYS TRIBUTE TO EX-NOMADS COACH MUNDE
The Football Association of Malawi (FAM) president Walter Nyamilandu Manda has paid tribute to former Be Forward Wanderers Coach and Malawi
Former Flames player and BE FORWARD Wanderers coach, Kannock Bruno Munde has died.
Wanderers has officially communicated about the tragedy.
#MHSRIP
The owner of Ntopwa, Isaac Jomo Osman, has been arrested and up to now charges placed on him are yet to be known.
Upon arrival yesterday at Limbe Police Station, Osman broke into tears.
Follow English Premier League on Owinna.com
Ntopwa owner, Isaac Jomo Osman, has been rearrested by police for offences yet to be revealed by Malawi Police Service (MPS).
Mtsogoleri wa bungwe la FAM, Walter Nyamilandu, wapempha anthu okonda masewero kuti adekhe pomwe ati amaliza ndondomeko zonse zoyenereza masewero kuyamba mdziko muno.
The newly appointed Minister of Youth and Sports, Ulemu Msungama, says his ministry will continue previous government-led sports projects.
Nduna ya achinyamata komanso masewero, Ulemu Msungama, yati ilunjika posintha ndondomeko zoyendetsera masewero mdziko muno ndi cholinga choti masewero osiyanasiyana apite patsogolo.
News
Ntopwa FC boss Isaac Jomo Osman has been arrested again for other offenses. Police have confirmed the arrest.ย
The newly appointed Minister of Youth and Sports, Ulemu Msungama, is on record saying FAM President, Walter Nyamilandu, has failed to improve the country's football standards.
Former Karonga United Chairman, Alufeyo Banda, will contest in the forthcoming NRFA elections on the post of the Vice Chairperson.
Flames defender, Charles Petro, shines in Moldova after playing 2 games for FC Sherrif since restart of games last week.
Resumption of football competitions in Mozambique is uncertain as the government has enforced another 30 days of lockdown amidst Covid-19.
Malawi President, Dr Lazarus Chakwera, has appointed Ulemu Msungama as the new Minister of Youth and Sports.
This is according to a statement released by Chief Secretary to the government.
Super League of Malawi (Sulom) is strategizing how best it can sell tickets if government allows people to watch games when football competitions resume.
Bungwe la FAM, pamodzi ndi nthambi zokhudzidwa, akulephera kuonetsetsa kuti masewero a mpira wa miyendo sakuseweredwa m'maboma molingana ndi chiletso chomwe chinaikidwa.
Bloemfontein Celtic have appointed former Flames player, John Maduka, as new head coach.
Maduka will be deputised by Abram Nteo while Simon Gopane is now goalkeepers trainer.
Congrats to John Maduka. One of Malawi's finest!
Owinna yasintha kaonekedwe kuti mudzitsatira ndi kucheza za mpira mosavuta.
Sankhani timu imene mumasapota ndi kutumiza nkhani za mpira pano pa Owinna.com lero.
Football Association of Malawi (FAM) is still waiting for government decision for football to resume amidst Covid-19.
FAM President, Walter Nyamilandu, made the remarks in an interview.
Timu ya Dedza Dynamos yomwe imasewera m'chigawo cha pakati pansi pa bungwe la CRFA layamika FAM kaamba kathandizo lomwe akupereka ku matimu kutsatira matenda a Covid-19.
In the wake of Corona Virus, it is confirmed that the country will not hold any independence celebrations which include hosting of a football game.
Kampani zomwe zikumanga mabwalo a Nyasa Big Bullets komanso BE FORWARD Wanderers zayamba zasiya kaye kugwira ntchito yawo yomanga mabwalowa.
Bungwe loyendetsa masewero a mpira wa miyendo mdziko muno la FAM lati likhala likupereka thandizo kwa matimu pakati pa mliri wa Corona Virus kwa miyezi pafupifupi isanu ndi iwiri ikubwera.