Login with Facebook to post predictions, updates & live scores
Please note that Charles Petro is still in Moldova doing trials at FC Sheriff Tiraspol.
Petrol will finish the trials on 15 February.
Blue Eagles have lost 1 nill to Lupembe Select in a friendly match.
Khumbo Chunda scored the lone goal for Lupembe Select.
Blue Eagles have commenced 2020 football preparations with friendly games.
Timu ya Blue Eagles yati m'masewero omwe ali nawo m'chigawo cha kumpoto apeza wosewera ena oti atumikire timuyi mu 2020.
Wapampando wa Blue Eagles, Alexander Ngwala, ndiye wanena izi.
Nyasa Big Bullets Reserve will start 2020 football preparations on Tuesday.
Head coach for the team, Enos Chatama, has confirmed the development.
Osewera wa Silver Strikers, Khuda Ikenna Muyaba, anali mdziko muno pomwe amazatsanzika komanso kutenga katundu okayambira umoyo wina ku South Africa. Muyaba akhala akusewelera timu ya Polokwane City.
Flames and Nyasa Big Bullets captain, John Lanjesi, will miss the opening of 2020 football season.
Lanjesi will be back on pitch in April this year.
Masapota apempha bungwe la Sulom kuti lichite zokambirana ndi kampani ya TNM kuti aonjezere ndalama zomwe matimu komanso wosewera amalandira akachita bwino season ili yonse.
Bungwe loyendetsa masewero a mpira mdziko muno la FAM lero lichititsa maphunziro a ndondomeko ya Club Licensing.
Maphunzirowa achitikira mu mzinda wa Blantyre motsogozedwa ndi mkulu wa ndondomeko-yi.
Blue Eagles will this weekend play against Lupembe and Chitipa Select in the northern part of Malawi.
Media Officer of Blue Eagles, Steve Kumalonje, has confirmed the development to Owinna.
Timu ya Civil Service yati ndiyokonzeka kumulandira Muhammad Sulumba kutumikira timuyi mu 2020.
Oyang'anira wosewera a timuyi, Gabriel Chirwa, ndiye wanena izi.
UD Songo and Chicken are the visiting teams in Nyasa Big Bullets Bonanza.
The two teams will join the host, Bullets and BE FORWARD Wanderers.
Civil Sporting has changed its name to Civil Service Football Club.
The change follows recommendation by the club sponsors.
Malawi Senior Men’s National team coach Meke Mwase has named 30 players to start non- residential training on Tuesday in preparation for back to back 2021 AFCON and World Cup games.
Timu ya Wanderers ichitititsa chisankho chake cha komiti yaikulu ya masapota pa 2 February.
Wapampando wa Wanderers, Gift Mkandawire, watsimikiza za izi.
Hassan Kajoke and Precious Sambani of Nyasa Big Bullets are travelling to Ukraine for trials.
The duo are set to do the trials at FC Rukh Lviv in the country.
The two will process their visas in Kenya.
Timu ya Silver Strikers yati ionjezera wosewera ena omwe atumikire timuyi chaka chino.
Mlembi wa timuyi, Innocent Kadamanja, wanena izi kutsatira kuchoka kwa Khuda Muyaba kupita ku South Africa.
Former Silver Strikers hit man, Khuda Muyaba, is currently the highest sold player in 2020 Football Season.
Muyaba who will be playing for Polokwane City for 4 years has been sold at 15,000,000.
The Football Association of Malawi in collaboration with National Football Coaches Association is currently conducting a CAF B Coaching Course Manual development workshop at Kris Star lodge, Blantyre.
Timu ya Wanderers yati wosewera omwe anali pa ngongole ndi matimu ena awatenga kuti atumikire timuyi chaka chino.
Wapampando wa timuyi, Gift Mkandawire, ndiye wanena izi.
Bungwe la FAM lati lionetsetsa kuti lamulo la Club Licensing matimu akulitsatira chaka chino.
Malingana ndi bungweli aphunzitsi amatimu akuyenera kukhala ndi mapepala oyenera.
Former Silver Strikers hit man, Khuda Muyaba, has secured a deal with Polokwane City in South Africa.
Owinna can reveal that the 2019 Airtel and TNM top goal scorer has signed a 4 year contract.
Timu ya Ntopwa iyamba zokonzekera zake Lolemba likudza-li.
Ntopwa yasintha tsiku loyambira zokonzekerazi kuchoka pa 3 February kufikira mwezi uno.Timuyi izichita zokonzekera zake pa bwalo la Kamuzu.
Ekwendeni Hammers will unveil their new technical panel this week.
Official for the team, Benjamin Thole, has revealed this to Owinna.
During the campaign period, FAM President Walter Nyamilandu, said time has come for Malawi to play in World Cup.
We believe for this to happen the team needs to have good preparations.
2019 Best Centre Referee Award - Newton Nyirenda (100,000 Kwacha), 2019 Best Second Referee - Elizabeth Sichinga (100,000 Kwacha), 2019 Best First Assistant Referee - Joseph Nyauti (100,000 Kwacha).
2019 Airtel Top 8 Top Goal Scorer
2019 TNM Super League Award
Silver Strikers have received 3,500,000 Kwacha for finishing on position 4 in TNM Super League.
2019 Best Technical Panel Management - 100,000 Kwacha
2019 Best Midfielder Award - 100,000 Kwacha
Blue Eagles have received 4,000,000 Kwacha for finishing on position 3.
2019 Fair Play Team Award - 800,000 Kwacha
2019 Most Improved Player Award - 100,000 Kwacha
Wanderers have received 7,000,000 for finishing on position 2 in TNM Super League.
2019 Best Defender - 100,000 Kwacha
2019 Best Goalkeeper - 100,000 Kwacha
2019 Player of the Season - 300,000 Kwacha
2019 TNM Super League Champions - 15,000,000 Kwacha
2019 Best Team Management Award - 1,000,000 Kwacha
2019 Disciplined Supporters - Nyasa Big Bullets Fans from Zomba (200,000 Kwacha)
Malawi National Football Team has been drawn in group D at 2022 FIFA World Cup Qualifiers.
Below is the complete set of the group.
Cameroon Ivory Coast Mozambique Malawi
Football Association of Malawi (FAM) has apopinted, Clement Kafwafwa as new team manager for Malawi National Football Team.
Wosewera wa Leeds United yemwe ndinzinka ya dziko lino, Henri Kumwenda, wakana kuzasewelera Flames. Henri wauza nyumba zina zofalitsa nkhani m'dziko muno kuti pano alibe chidwi chosewelera timuyi.
Flames will know their 2022 FIFA World Cup Qualifiers group opponents today.
The draw is scheduled to take place in Cairo, Egypt this evening.
Matimu a Mzuzu Warriors ndi Ekwendeni Hammers akana malipoti omwe akumveka kuti akufuna apange mgwirizano ndi timu ya Masters Security.
Boma tsopano labwera poyera pomwe lati ntchito yomanga mabwalo a Bullets ndi Wanderers iyambika mu February.
Nduna ya zamasewero, Francis Phiso, yatsimikiza za nkhaniyi.
Nyasa Big Bullets has set date for the club's award ceremony for this year.
Speaking to Owinna, Chief Administrative Officer, Albert Chigoga, said they will hold the ceremony on 7th March.
Wosewera wa Silver Strikers, Khuda Muyaba, ali m'dziko la South Africa komwe akukayetsa mwayi ku Polakwane City.
Muyaba wanyamuka m'dziko muno Loweluka lapitali.
The following are teams that will participate 2020 FAM Charity Shield.
- Nyasa Big Bullets, Silver Strikers, Blue Eagles and BE FORWARD Wanderers.
BE FORWARD Wanderers will play 2020 FAM Charity Shield despite not lifting a trophy in 2019.
FAM Communication and Competitions Manager, Gomegzani Zakazaka, has confirmed this to Owinna.
Nyasa Big Bullets will hold it's yearly bonanza in February.
One of senior officials at the club, Albert Chigoga, confirmed about the development.
FAM yayamba zokambirana ndi bungwe la Sulom pomwe akufuna kupereka bwalo la Chilomoni ku bungwe-li.
Akuluakulu ena a bungwe la FAM auza izi Owinna.
Masters Security FC has changed its name to Masters Borehole Drilling FC.
Alfred Gangata, has confirmed the development to Owinna.